Deuteronomo 1:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Tipite kuti? Abale athu achititsa mantha mitima yathu+ potiuza kuti: “Kumeneko tinaonako anthu akuluakulu, ndiponso aatali kuposa ifeyo,+ ndi mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri yofika kumwamba.+ Kumeneko tinaonakonso ana a Anaki.”’+ Yoswa 2:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndipo iye anauza amunawo kuti: “Ndikudziwa kuti Yehova akupatsani ndithu dziko lino.+ Ife tagwidwa ndi mantha chifukwa cha inu,+ ndipo anthu a dziko lino ataya mtima chifukwa chokuopani.+ Yoswa 7:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Ndipo amuna a ku Aiwo anapha amuna achiisiraeli pafupifupi 36. Anawathamangitsabe+ kuchokera kuchipata mpaka ku Sebarimu, n’kupitiriza kuwapha mpaka pamalo otsetsereka. Zitatero, mitima ya Aisiraeli onse inasungunuka ndi mantha.+ 1 Samueli 17:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Sauli+ ndi Aisiraeli onse atamva mawu a Mfilisitiwa anaopsezedwa ndipo anachita mantha kwambiri.+
28 Tipite kuti? Abale athu achititsa mantha mitima yathu+ potiuza kuti: “Kumeneko tinaonako anthu akuluakulu, ndiponso aatali kuposa ifeyo,+ ndi mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri yofika kumwamba.+ Kumeneko tinaonakonso ana a Anaki.”’+
9 Ndipo iye anauza amunawo kuti: “Ndikudziwa kuti Yehova akupatsani ndithu dziko lino.+ Ife tagwidwa ndi mantha chifukwa cha inu,+ ndipo anthu a dziko lino ataya mtima chifukwa chokuopani.+
5 Ndipo amuna a ku Aiwo anapha amuna achiisiraeli pafupifupi 36. Anawathamangitsabe+ kuchokera kuchipata mpaka ku Sebarimu, n’kupitiriza kuwapha mpaka pamalo otsetsereka. Zitatero, mitima ya Aisiraeli onse inasungunuka ndi mantha.+