Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno panali Agadi ena amene anasankha kupita kumbali ya Davide m’chipululu,+ kumalo ovuta kufikako. Amenewa anali amuna amphamvu ndi olimba mtima, asilikali okonzekera nkhondo, amene zishango zawo zazikulu ndi mikondo yawo ing’onoing’ono zinkakhala zokonzeka.+ Nkhope zawo zinali ngati nkhope za mikango,+ ndipo liwiro lawo linali ngati la mbawala m’mapiri.+

  • Nyimbo ya Solomo 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mpaka nthawi ya kamphepo kayaziyazi ndiponso mpaka mithunzi itachoka, tembenuka wachikondi wanga. Ukhale ngati mbawala+ kapena ngati mphoyo yaing’ono pamapiri amene akutilekanitsa.

  • Nyimbo ya Solomo 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Thamanga wachikondi wanga. Ukhale ngati insa kapena ngati mphoyo yaing’ono pamapiri pamene pamamera maluwa onunkhira.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena