Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 13:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Panthawiyi n’kuti Abisalomu atathawa.+ Pambuyo pake mnyamata wina amene anali mlonda,+ anakweza maso ndipo anaona anthu ambiri akubwera kumbuyo kwake mumsewu umene unali m’mphepete mwa phiri.

  • 2 Mafumu 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ku Yezereeliko,+ mlonda+ amene anaimirira pansanja+ anaona gulu lankhondo la Yehu likubwera mwaliwiro. Nthawi yomweyo mlondayo anati: “Ndikuona gulu la amuna likubwera mwaliwiro.” Pamenepo Yehoramu anati: “Uza munthu wokwera hatchi kuti apite kukakumana nawo. Akawafunse kuti, ‘Kodi mukubwerera zamtendere?’”+

  • Yesaya 21:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pakuti Yehova wandiuza kuti:

      “Pita, kaike mlonda pamalo ake, kuti anene zonse zimene aone.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena