Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 14:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 ndipo ndinang’amba+ ufumuwo kuuchotsa kunyumba ya Davide ndi kuupereka kwa iwe, koma iwe sunakhale ngati Davide mtumiki wanga. Iyeyo anasunga malamulo anga ndi kunditsatira ndi mtima wake wonse mwa kuchita zinthu zoyenera zokhazokha m’maso mwanga.+

  • 2 Mafumu 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yosiya anachita zoyenera pamaso pa Yehova+ ndipo anayenda m’njira zonse za Davide kholo lake.+ Iye sanapatukire mbali ya kudzanja lamanja kapena lamanzere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena