-
Yobu 34:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Akaika mtima wake pa munthu aliyense,
Akatenga mzimu* ndi mpweya wa munthuyo,+
-
Mlaliki 9:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Nditaganizanso ndinaona kuti padziko lapansi pano anthu othamanga kwambiri sapambana pampikisano,+ amphamvu sapambana pankhondo,+ anzeru sapeza chakudya,+ omvetsa zinthu nawonso sapeza chuma,+ ndipo ngakhale odziwa zinthu sakondedwa,+ chifukwa nthawi yatsoka ndi zinthu zosayembekezereka zimagwera onsewo.+
-
-
-