Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mwana wa Solomo anali Rehobowamu.+ Rehobowamu anabereka Abiya,+ Abiya anabereka Asa,+ Asa anabereka Yehosafati,+

  • 2 Mbiri 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndiyeno Yehosafati+ mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwake, ndipo analimbitsa ufumu wake mu Isiraeli.

  • 2 Mbiri 20:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Yehosafati+ anapitiriza kulamulira ku Yuda. Iye anali ndi zaka 35 pamene anayamba kulamulira ndipo analamulira ku Yerusalemu zaka 25. Mayi ake dzina lawo linali Azuba+ mwana wa Sili.

  • Mateyu 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Asa anabereka Yehosafati.+

      Yehosafati anabereka Yehoramu.+

      Yehoramu anabereka Uziya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena