-
2 Mbiri 1:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Pamenepo Mulungu anauza Solomo kuti: “Chifukwa chakuti zimenezi ndi zimene zili mumtima mwako+ ndipo sunapemphe katundu, chuma ndi ulemu kapenanso moyo wa anthu amene amadana nawe, sunapemphenso kuti ukhale ndi moyo masiku ambiri,+ koma wapempha kuti ukhale ndi nzeru ndi luntha lodziwa zinthu kuti uweruze anthu anga amene ndakupatsa kuti ukhale mfumu yawo,+
-