Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Musakumbukire machimo a pa unyamata wanga ndi zolakwa zanga.+

      Ndikumbukireni malinga ndi kukoma mtima kwanu kosatha,+

      Ndiponso chifukwa cha ubwino wanu, inu Yehova.+

  • Maliko 3:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndithu ndikukuuzani, ana a anthu adzakhululukidwa zinthu zonse, kaya ndi machimo otani amene anachita kapena mawu onyoza otani amene analankhula.+

  • Luka 23:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 [[Koma Yesu anati: “Atate, akhululukireni,+ chifukwa sakudziwa chimene akuchita.”]]* Ndipo iwo anagawana malaya ake mwa kuchita maere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena