-
2 Mbiri 9:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Adalitsike Yehova Mulungu wanu,+ amene wasangalala+ nanu mwa kukuikani pampando wake wachifumu+ monga mfumu yolamulira m’malo mwa Yehova Mulungu wanu.+ Popeza Mulungu wanu anakonda+ Isiraeli kuti akhalepo mpaka kalekale, wakuikani kuti mukhale mfumu yawo,+ kuti muzipereka zigamulo+ ndi kuchita chilungamo.”+
-