Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Zekariya 14:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pa tsiku limenelo mapazi ake adzaponda paphiri la mitengo ya maolivi. Phiri limeneli lili moyang’anizana ndi Yerusalemu kumbali ya kum’mawa.+ Phiri la mitengo ya maolivi+ limeneli lidzagawanika pakati+ kuyambira kum’mawa mpaka kumadzulo. Zikadzatero, pakati pa mapiriwo padzakhala chigwa chachikulu kwambiri. Hafu imodzi ya phirilo idzasunthira kumpoto ndipo hafu inayo idzasunthira kum’mwera.

  • Machitidwe 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pamenepo anabwerera+ ku Yerusalemu, kuchokera kuphiri lotchedwa phiri la Maolivi. Phiri limeneli lili pafupi ndi Yerusalemu, pa mtunda wa ulendo wa tsiku la sabata.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena