Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 24:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mfumuyo inatenga+ anthu onse a ku Yerusalemu, akalonga onse,+ amuna onse amphamvu ndi olimba mtima,+ mmisiri aliyense+ ndi munthu aliyense womanga makoma achitetezo, n’kupita nawo ku Babulo. Anthu onse amene inawatenga analipo 10,000. Palibe amene anatsala, kupatulapo anthu onyozeka+ okha a m’dzikolo.

  • Yeremiya 39:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndiyeno ena mwa anthuwo, anthu onyozeka amene analibe kalikonse, Nebuzaradani mkulu wa asilikali olondera mfumu anawasiya m’dziko la Yuda,+ ndipo pa tsiku limenelo anawapatsa minda ya mpesa ndi ntchito zokakamiza kuti azigwira.+

  • Yeremiya 40:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Patapita nthawi, akuluakulu onse a magulu ankhondo amene anali m’madera a kunja kwa mzinda+ pamodzi ndi anthu awo, anamva kuti mfumu ya Babulo yaika Gedaliya mwana wa Ahikamu kukhala wolamulira dzikolo. Anamvanso kuti yamuika kuti azilamulira amuna, akazi, ana ndi anthu onyozeka m’dzikolo amene sanatengedwe kupita ku ukapolo ku Babulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena