-
Nehemiya 9:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 “Tsopano Mulungu wathu, Mulungu wamkulu,+ wamphamvu+ ndi wochititsa mantha,+ wosunga pangano+ ndi kusonyeza kukoma mtima kosatha,+ musachepetse+ mavuto onse amene agwera ifeyo,+ mafumu athu,+ akalonga athu,+ ansembe athu,+ aneneri athu,+ makolo athu+ ndi anthu anu onse kuchokera masiku a mafumu a Asuri mpaka lero.+
-