Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Tsopano munthu winawake dzina lake Namani,+ mkulu wa gulu la asilikali a mfumu ya Siriya, anakhala munthu wofunika pamaso pa mbuye wake. Iye anali wolemekezeka, chifukwa Yehova anapulumutsa Siriya+ kudzera mwa iyeyo. Munthuyo anasonyeza kuti anali wamphamvu ndi wolimba mtima, ngakhale kuti anali wakhate.

  • Luka 4:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ndiponso, munali akhate ambiri mu Isiraeli m’nthawi ya mneneri Elisa. Komabe palibe aliyense wa iwo amene anayeretsedwa, koma Namani, mwamuna wa ku Siriya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena