6 Koma iwo anati: “Sitingamwe vinyo, chifukwa Yonadabu mwana wa Rekabu,+ kholo lathu, anatilamula kuti, ‘Inuyo kapena ana anu musamamwe vinyo mpaka kalekale.+
19 Yehova wa makamu, Mulungu wa Isiraeli wanena kuti: “Sipadzasowa munthu wa m’banja la Yonadabu mwana wa Rekabu woima+ pamaso panga kuti azinditumikira nthawi zonse.”’”+