Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 24:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Akalonga onse+ ndi anthu onse anayamba kusangalala,+ ndipo anali kubweretsa ndalama za msonkhowo n’kumaziponya m’bokosi+ lija kufikira aliyense anapereka.

  • Mateyu 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 kuti mphatso zako zachifundo zikhale zamseri. Ukatero Atate wako amene akuyang’ana kuseriko adzakubwezera.+

  • 2 Akorinto 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Aliyense achite mogwirizana ndi mmene watsimikizira mumtima mwake, osati monyinyirika+ kapena mokakamizika, chifukwa Mulungu amakonda munthu wopereka mokondwera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena