Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 “Matemberero onsewa+ adzakugwera, kukutsatira ndi kukupeza kufikira utafafanizika,+ chifukwa sunamvere mawu a Yehova Mulungu wako mwa kusunga malamulo ndi mfundo zake zimene anakupatsa.+

  • 2 Mafumu 18:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho Hezekiya mfumu ya Yuda anatumiza uthenga kwa mfumu ya Asuri ku Lakisi, wakuti: “Ndachimwa. Siyani kundiukira. Ndikupatsani chilichonse chimene mungandilamule.”+ Chotero mfumu ya Asuri inalamula Hezekiya mfumu ya Yuda kuti apereke matalente* 300 a siliva+ ndi matalente 30 a golide.

  • Ezara 7:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Amuna inu mudziwe kuti ansembe,+ Alevi,+ oimba,+ alonda a pakhomo,+ Anetini,+ ndi anthu ogwira ntchito panyumba ya Mulunguyi, musawakhometse msonkho umene munthu aliyense amakhoma, msonkho wakatundu,+ kapena msonkho wapanjira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena