Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Siliva, golide, ndi zipangizo zamkuwa ndi zachitsulo, zonse n’zopatulika kwa Yehova.+ Ziyenera kupita ku chuma cha Yehova.”+

  • 1 Mbiri 29:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Ndine ndani ine,+ ndipo anthu anga ndani kuti tithe kupereka nsembe zaufulu ngati zimenezi?+ Pakuti chilichonse n’chochokera kwa inu,+ ndipo tapereka kwa inu zochokera m’dzanja lanu.

  • 2 Mbiri 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pa mapeto pake, Solomo anamaliza ntchito yonse ya panyumba ya Yehova imene anayenera kugwira.+ Kenako Solomo anayamba kubweretsa zinthu zimene Davide bambo ake+ anaziyeretsa. Siliva, golide, ndi ziwiya zonse anaziika mosungira chuma cha panyumba ya Mulungu woona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena