-
1 Mbiri 26:26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
26 Selomoti ameneyu pamodzi ndi abale ake anali kuyang’anira chuma chonse cha zinthu zimene anaziyeretsa kukhala zopatulika. Amene anayeretsa zinthu zimenezi kukhala zopatulika+ anali Davide+ mfumu, atsogoleri a nyumba za makolo,+ atsogoleri a magulu a anthu 1,000, a magulu a anthu 100, ndi atsogoleri a asilikali.
-