Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 31:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Tsopano lolani kuti aliyense wa ife apereke zimene wabwera nazo monga chopereka kwa Yehova,+ zinthu zagolide, matcheni ovala m’miyendo, zibangili, mphete zachifumu,+ ndolo,* ndi zodzikongoletsera zina za akazi.+ Tipereke zimenezi kwa Yehova kuti ziphimbe machimo athu.”

  • 1 Mbiri 18:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Zinthu zimenezi Mfumu Davide inazipatulira+ Yehova pamodzi ndi siliva ndi golide amene inalanda ku mitundu yonse,+ kuchokera ku Edomu, ku Mowabu,+ kwa ana a Amoni,+ Afilisiti,+ ndi Aamaleki.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena