Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Adalitsike Yehova Mulungu wa Isiraeli kuyambira kalekale mpaka kalekale.’”+

      Ndiyeno anthu onse ananena kuti, “Ame!”* n’kutamanda Yehova.+

  • Salimo 134:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pamene mukupemphera mutakweza manja anu, muzikhala oyera,+

      Ndipo tamandani Yehova.+

  • Salimo 145:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 145 Ndidzakukwezani, inu Mfumu ndi Mulungu wanga,+

      Ndipo ndidzatamanda dzina lanu mpaka kalekale, ndithu mpaka muyaya.+

  • Aefeso 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Atamandike Mulungu, Atate wa Ambuye wathu Yesu Khristu,+ pakuti watidalitsa+ ndi dalitso lililonse lauzimu m’malo akumwamba+ mogwirizana ndi Khristu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena