Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 19:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Koma anthu a ku Isiraeli anayankha anthu a ku Yuda kuti: “Ifetu tili ndi mafuko 10 mu ufumu umenewu.+ Choncho mu ufumu wa Davide tilitu ndi mphamvu zambiri kuposa inu. Ndiyeno n’chifukwa chiyani mukutinyoza chotero, ndipo kodi ife sitinayenera kukhala patsogolo+ pobweretsa mfumu yathu?” Koma mawu a anthu a ku Yuda anali aukali kwambiri kuposa a anthu a ku Isiraeli.

  • Miyambo 29:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Munthu wokonda kukwiya amayambitsa mkangano,+ ndipo aliyense wokonda kupsa mtima amakhala ndi machimo ambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena