Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 13:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kenako Mose anagawira dziko fuko la ana a Gadi potsata mabanja awo.+

  • Yoswa 13:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Gawo lawolo linaphatikizaponso mizinda ya m’chigwa ya Beti-harana,+ Beti-nimira,+ Sukoti,+ Zafoni, ndi mbali yotsala ya dziko la Sihoni mfumu ya Hesiboni.+ Mtsinje wa Yorodano ndiwo unali malire awo mpaka kunyanja ya Kinereti.+ Gawo lawo linali kum’mawa kwa mtsinje wa Yorodano.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena