Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Fuko la Manase linapatsidwa magawo 10, kuwonjezera pa dera la Giliyadi ndi Basana lomwe linali kutsidya lina la Yorodano.+

  • Yoswa 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Malire a gawo la fuko la Manase anayambira ku Aseri kukafika ku Mikametatu,+ patsogolo pa Sekemu.+ Malirewo analowera kumanja kukafika kwa anthu okhala ku Eni-Tapuwa.

  • 2 Mbiri 30:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anthu+ ochokera ku Aseri, ku Manase, ndi ku Zebuloni okha ndi amene anadzichepetsa+ n’kubwera ku Yerusalemu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena