2 Mbiri 30:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Asilikali othamangawo+ anapitiriza ulendo wawo ndipo anapita kumzinda ndi mzinda m’dziko lonse la Efuraimu+ ndi Manase mpaka ku Zebuloni. Koma anthuwo ankangokhalira kuwatonza ndi kuwaseka.+ Salimo 35:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Anthu ampatuko amene anali kunditonza kuti apeze kachakudya,+Anandikukutira mano.+
10 Asilikali othamangawo+ anapitiriza ulendo wawo ndipo anapita kumzinda ndi mzinda m’dziko lonse la Efuraimu+ ndi Manase mpaka ku Zebuloni. Koma anthuwo ankangokhalira kuwatonza ndi kuwaseka.+