Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno Mose anakaima pachipata cha msasawo, ndipo anati: “Ndani ali kumbali ya Yehova? Abwere kwa ine!”+ Ndipo ana onse aamuna a Levi anayamba kusonkhana kwa Mose.

  • Deuteronomo 33:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndipo kwa Levi anati:+

      “Tumimu ndi Urimu+ wanu ndizo za munthu wokhulupirika kwa inu,+

      Amene munamuyesa pa Masa.+

      Munayamba kulimbana naye pafupi ndi madzi a Meriba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena