Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Akanani ndi anthu onse a m’dziko lino adzamva zimenezi, ndipo adzatizinga ndithu, ndi kufafaniza dzina lathu kulichotsa padziko lapansi.+ Nanga zikatero mudzaliteteza bwanji dzina lanu lalikulu?”+

  • 1 Samueli 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mapazi a okhulupirika ake amawateteza.+

      Koma anthu oipa amawawononga mu mdima,+

      Pakuti munthu sakhala wapamwamba chifukwa cha mphamvu zake.+

  • Salimo 9:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nyamukani, inu Yehova! Munthu asakuposeni mphamvu.+

      Anthu a mitundu ina aweruzidwe pamaso panu.+

  • Mateyu 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Koma inu muzipemphera motere:+

      “‘Atate wathu wakumwamba, dzina+ lanu liyeretsedwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena