Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Davide anapitiriza kulamulira Isiraeli+ yense ndipo nthawi zonse anali kupereka zigamulo ndi kuchita chilungamo+ kwa anthu ake onse.+

  • 1 Mafumu 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Chotero Solomo anayamba kuchita zinthu zimene zinali zoipa+ m’maso mwa Yehova, ndipo sanatsatire Yehova ndi mtima wonse ngati Davide bambo ake.+

  • 1 Mafumu 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Abiyamu anapitiriza kuyenda m’machimo onse amene bambo ake anachita. Sanatumikire Yehova Mulungu wake ndi mtima wathunthu+ ngati mmene anachitira Davide kholo lake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena