Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Ndikukupemphani inu Yehova, chonde kumbukirani+ kuti ndinayenda+ pamaso panu mokhulupirika+ ndiponso ndi mtima wathunthu,+ komanso ndinachita zabwino pamaso panu.”+ Kenako Hezekiya anayamba kulira kwambiri.+

  • 2 Mbiri 25:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Amaziya anapitiriza kuchita zolungama pamaso pa Yehova,+ koma osati ndi mtima wathunthu.+

  • 2 Mbiri 31:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Hezekiya anachita zimenezi mu Yuda yense, ndipo anapitiriza kuchita zabwino,+ zoyenera+ ndi zokhulupirika+ pamaso pa Yehova Mulungu wake.

  • Salimo 119:80
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  80 Mtima wanga usunge malangizo anu mosalakwitsa kanthu,+

      Kuti ndisachite manyazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena