Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 2:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma ine ndinawayankha kuti: “Mulungu wakumwamba+ ndi amene adzatithandiza kuti zinthu zitiyendere bwino,+ ndipo ife atumiki ake tipitiriza kumanga mpandawu. Inu mulibe gawo,+ ufulu kapena chilichonse chokukumbukirani nacho+ mu Yerusalemu.”

  • Yohane 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mayi wachisamariyayo anafunsa Yesu kuti: “Popeza inu ndinu Myuda, bwanji mukupempha madzi akumwa kwa ine, mayi wachisamariya?” (Pakuti Ayuda ndi Asamariya sayanjana.)+

  • Yohane 4:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Inu mumalambira chimene simuchidziwa.+ Ife timalambira chimene tikuchidziwa, chifukwa chipulumutso chikuchokera kwa Ayuda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena