Ezara 1:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Aliyense amene ali pakati panu mwa anthu onse amene amamutumikira, Mulungu wake akhale naye.+ Choncho apite ku Yerusalemu m’dziko la Yuda n’kukamanganso nyumba ya Yehova Mulungu wa Isiraeli, yomwe inali ku Yerusalemu.+ Iye ndiye Mulungu woona.+ Ezara 5:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndiyeno ife tinafunsa akuluakulu amenewo kuti: ‘Kodi ndani wakulamulani kuti mumange nyumbayi ndi kumaliza khoma lamatabwali?’+
3 Aliyense amene ali pakati panu mwa anthu onse amene amamutumikira, Mulungu wake akhale naye.+ Choncho apite ku Yerusalemu m’dziko la Yuda n’kukamanganso nyumba ya Yehova Mulungu wa Isiraeli, yomwe inali ku Yerusalemu.+ Iye ndiye Mulungu woona.+
9 Ndiyeno ife tinafunsa akuluakulu amenewo kuti: ‘Kodi ndani wakulamulani kuti mumange nyumbayi ndi kumaliza khoma lamatabwali?’+