Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 28:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako Davide anauza Solomo mwana wake kuti: “Limba mtima,+ ugwire ntchitoyi mwamphamvu. Usaope+ kapena kuchita mantha+ chifukwa Yehova Mulungu, Mulungu wanga, ali ndi iwe.+ Sadzakutaya+ kapena kukusiya, kufikira ntchito yonse yokhudza utumiki wa nyumba ya Yehova itatha.

  • Salimo 145:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova ali pafupi ndi onse oitanira pa iye.+

      Iye ali pafupi ndi onse amene amamuitana m’choonadi,+

  • Yesaya 45:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Ine ndautsa winawake m’chilungamo+ ndipo njira zake zonse ndidzaziwongola.+ Iye ndi amene adzamange mzinda wanga+ ndipo anthu anga amene ali ku ukapolo adzawamasula,+ koma osati ndi malipiro+ kapena ndi chiphuphu,” watero Yehova wa makamu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena