Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 8:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako ndinalamula kuti tisale kudya tili kumtsinje wa Ahava kuja, kuti tidzichepetse+ pamaso pa Mulungu wathu ndi kumupempha kuti atisonyeze njira yoyenera+ kwa ife, ana athu,+ ndi katundu wathu yense.

  • Ezara 8:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Pomalizira pake tinachoka pamtsinje wa Ahava+ pa tsiku la 12 la mwezi woyamba+ kuti tipite ku Yerusalemu. Dzanja la Mulungu wathu linali nafe pa ulendowu moti anatipulumutsa+ m’manja mwa adani ndiponso kwa achifwamba a m’njira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena