Salimo 79:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Bwezerani anthu oyandikana nafe mwa kuwatsanulira chitonzo pachifuwa pawo maulendo 7,+Inu Yehova, muwabwezere chitonzo chimene anachita pa inu.+ Miyambo 3:34 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 34 Onyoza,+ iye amawanyoza,+ koma ofatsa amawakomera mtima.+
12 Bwezerani anthu oyandikana nafe mwa kuwatsanulira chitonzo pachifuwa pawo maulendo 7,+Inu Yehova, muwabwezere chitonzo chimene anachita pa inu.+