Nehemiya 4:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Tsopano Tobia+ Muamoni,+ anali pamodzi ndi Sanibalati ndipo anati: “Ngakhaletu nkhandwe+ itakwera pampanda wamiyala umene akumangawo ingathe kuugwetsa ndithu.” Nehemiya 6:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Inu Mulungu wanga, kumbukirani+ zinthu zonse zimene Tobia+ ndi Sanibalati anachita. Mukumbukirenso Nowadiya mneneri wamkazi+ ndi aneneri ena onse amene anali kuyesetsabe kundiopseza. Nehemiya 13:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ndiyeno ndinafika ku Yerusalemu ndipo ndinaona zoipa zimene Eliyasibu+ anachita mwa kukonzera Tobia+ chipinda m’bwalo la nyumba+ ya Mulungu woona.
3 Tsopano Tobia+ Muamoni,+ anali pamodzi ndi Sanibalati ndipo anati: “Ngakhaletu nkhandwe+ itakwera pampanda wamiyala umene akumangawo ingathe kuugwetsa ndithu.”
14 Inu Mulungu wanga, kumbukirani+ zinthu zonse zimene Tobia+ ndi Sanibalati anachita. Mukumbukirenso Nowadiya mneneri wamkazi+ ndi aneneri ena onse amene anali kuyesetsabe kundiopseza.
7 Ndiyeno ndinafika ku Yerusalemu ndipo ndinaona zoipa zimene Eliyasibu+ anachita mwa kukonzera Tobia+ chipinda m’bwalo la nyumba+ ya Mulungu woona.