Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 21:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kuchokera m’fuko la Benjamini, anawapatsa Gibeoni+ ndi malo ake odyetserako ziweto, Geba+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

  • 1 Mbiri 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Panalinso ana a Ehudi amene anali atsogoleri a nyumba za makolo a anthu okhala ku Geba.+ Iwowa anagwira anthu ndi kuwatengera ku Manahati.

  • Nehemiya 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ana a Benjamini anakhala ku Geba,+ Mikimasi,+ Aiya,+ Beteli+ ndi midzi yake yozungulira,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena