Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 21:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Rizipa mwana wamkazi wa Aya+ anatenga chiguduli+ ndi kuchiyala pamwala kuti azikhala pamenepo, kuyambira kuchiyambi kwa nyengo yokolola kufikira pamene mvula inagwa pamitemboyo kuchokera kumwamba.+ Iye sanalole mbalame+ zam’mlengalenga kutera pamitemboyo masana, ndipo usiku sanalole zilombo zakutchire+ kufikapo.

  • Yesaya 58:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kodi kusala kudya kumene ine ndasankha kukhale kotere? Kodi likhale tsiku loti munthu wochokera kufumbi azisautsa moyo wake?+ Kodi likhale tsiku loti munthu aziweramitsa mutu wake ngati udzu, ndiponso loti aziyala chiguduli ngati bedi lake n’kuwazapo phulusa?+ Kodi limeneli ndi limene mumalitcha tsiku losala kudya ndi lovomerezeka kwa Yehova?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena