Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano Hegai anasangalala naye mtsikanayu moti anam’sonyeza kukoma mtima kosatha.+ Mwamsanga anam’paka mafuta okongoletsa,+ anam’patsa chakudya chapadera ndiponso anam’patsa atsikana 7 osankhidwa kuchokera kunyumba ya mfumu. Kenako anam’samutsa pamodzi ndi atsikanawo n’kuwapatsa malo abwino kwambiri m’nyumba ya akaziyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena