Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 20:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kuti mfuu yachisangalalo ya anthu oipa sikhalitsa,+

      Ndiponso kuti kusangalala kwa wampatuko kumakhala kwa kanthawi?

  • Luka 6:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 “Tsoka inu amene mukukhuta tsopano, chifukwa mudzamva njala.+

      “Tsoka inu amene mukuseka tsopano, chifukwa mudzamva chisoni ndi kulira.+

  • Yakobo 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Imvani chisoni ndipo lirani.+ Kuseka kwanu kusanduke kulira, ndipo chisangalalo chanu chisanduke chisoni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena