Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 27:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ngakhale gulu lankhondo litamanga msasa kuti lindiukire,+

      Mtima wanga sudzachita mantha.+

      Ngakhale nkhondo yolimbana ndi ine itayambika,+

      Pameneponso ndidzadalira Mulungu.+

  • Salimo 139:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Inu Yehova, pajatu ine ndimadana ndi anthu amene amadana nanu kwambiri,+

      Ndipo anthu okupandukirani ndimanyansidwa nawo.+

  • Salimo 139:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndimadana nawo kwambiri.+

      Kwa ine akhala adani enieni.+

  • Mateyu 10:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Musachite mantha+ ndi amene amapha thupi koma sangaphe moyo, m’malomwake, muziopa iye+ amene angathe kuwononga zonse ziwiri, moyo ndi thupi lomwe m’Gehena.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena