Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Atatero, Farao anavula mphete yake yachifumu+ kudzanja lake, n’kuiveka kudzanja la Yosefe. Anamuvekanso malaya amtengo wapatali, ndi tcheni chagolide m’khosi mwake.+

  • Esitere 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 amubweretsere zovala zachifumu+ zimene mfumu imavala ndi hatchi* imene mfumu imakwera.+ Hatchiyo aiveke duku lachifumu.

  • Luka 16:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Munthu winawake+ anali wolemera, ndipo nthawi zonse anali kuvala zovala zofiirira zapamwamba ndi nsalu zabwino kwambiri. Iye anali kusangalala ndi kudyerera tsiku ndi tsiku.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena