Ekisodo 17:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Tsopano Yehova anauza Mose kuti: “Lemba zimenezi m’buku monga chikumbutso+ ndi kumuuza Yoswa kuti, ‘M’kupita kwa nthawi ndidzafafaniziratu Aamaleki padziko lapansi* ndipo sadzakumbukika n’komwe.’”+ Ekisodo 17:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 ndipo anati: “Popeza dzanja laukira mpando wachifumu+ wa Ya,+ Yehova adzamenya nkhondo ndi Aamaleki ku mibadwomibadwo.”+ Numeri 24:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Madzi odzaza mitsuko yake iwiri akutayikirabe pansi,Ndipo mbewu yake ili m’mbali mwa madzi ambiri.+Mfumu yakenso+ idzakwezeka kuposa Agagi,+Ndi ufumu wake udzakwezedwa.+ Salimo 21:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Mudzawononga ana awo kuwachotsa padziko lapansi,+Ndipo ana awo mudzawachotsa pakati pa ana a anthu.+ Salimo 109:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Mbadwa zake ziphedwe ndi kuchotsedwa m’dziko.+Dzina lawo lifafanizidwe mu m’badwo wotsatira.+
14 Tsopano Yehova anauza Mose kuti: “Lemba zimenezi m’buku monga chikumbutso+ ndi kumuuza Yoswa kuti, ‘M’kupita kwa nthawi ndidzafafaniziratu Aamaleki padziko lapansi* ndipo sadzakumbukika n’komwe.’”+
16 ndipo anati: “Popeza dzanja laukira mpando wachifumu+ wa Ya,+ Yehova adzamenya nkhondo ndi Aamaleki ku mibadwomibadwo.”+
7 Madzi odzaza mitsuko yake iwiri akutayikirabe pansi,Ndipo mbewu yake ili m’mbali mwa madzi ambiri.+Mfumu yakenso+ idzakwezeka kuposa Agagi,+Ndi ufumu wake udzakwezedwa.+
10 Mudzawononga ana awo kuwachotsa padziko lapansi,+Ndipo ana awo mudzawachotsa pakati pa ana a anthu.+