Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano Yehova anauza Mose kuti: “Lemba zimenezi m’buku monga chikumbutso+ ndi kumuuza Yoswa kuti, ‘M’kupita kwa nthawi ndidzafafaniziratu Aamaleki padziko lapansi* ndipo sadzakumbukika n’komwe.’”+

  • Ekisodo 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 ndipo anati: “Popeza dzanja laukira mpando wachifumu+ wa Ya,+ Yehova adzamenya nkhondo ndi Aamaleki ku mibadwomibadwo.”+

  • Numeri 24:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Madzi odzaza mitsuko yake iwiri akutayikirabe pansi,

      Ndipo mbewu yake ili m’mbali mwa madzi ambiri.+

      Mfumu yakenso+ idzakwezeka kuposa Agagi,+

      Ndi ufumu wake udzakwezedwa.+

  • Salimo 21:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mudzawononga ana awo kuwachotsa padziko lapansi,+

      Ndipo ana awo mudzawachotsa pakati pa ana a anthu.+

  • Salimo 109:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mbadwa zake ziphedwe ndi kuchotsedwa m’dziko.+

      Dzina lawo lifafanizidwe mu m’badwo wotsatira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena