Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho atumiki onse a mfumu amene anali kuchipata cha mfumu+ anali kuwerama ndi kugwadira Hamani, pakuti mfumu inali italamula kuti anthu azim’chitira zimenezi. Koma Moredekai sanali kumuweramira kapena kumugwadira.+

  • Esitere 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamenepo mkazi wake Zeresi ndi anzake onsewo anamuuza kuti: “Mukonzetse mtengo+ wotalika mikono* 50. Ndiyeno m’mawa+ mukauze mfumu kuti apachike Moredekai pamtengowo.+ Mukatero mupite kuphwando ndi mfumu muli wosangalala.” Zimenezi zinaoneka zosangalatsa+ kwa Hamani, choncho anakonzetsa mtengowo.+

  • Esitere 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Moredekai Myuda anali wachiwiri+ kwa Mfumu Ahasiwero ndipo anali wotchuka pakati pa Ayuda. Khamu lonse la abale ake linali kukondwera naye. Iye anali kuchitira zabwino anthu a mtundu wake ndi kulankhula zamtendere+ kwa ana awo onse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena