Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo ayasamula kukamwa kwawo kuti andimeze.+

      Andimenya mbama ndi mnyozo.

      Asonkhana ambirimbiri kuti alimbane nane.+

  • Yobu 17:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndithu, onyoza andizungulira,+

      Ndipo diso langa likuyang’anitsitsa khalidwe lawo lopanduka.

  • Yobu 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “Tsopano anthu amene ndi ana aang’ono poyerekeza ndi ine,+

      Akundiseka.+

      Anthu amene abambo awo sindikanalola

      Kuwaika pamodzi ndi agalu oweta nkhosa zanga.

  • Salimo 22:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anthu onse ondiona amandinyodola.+

      Iwo amandinyogodola ndi pakamwa pawo, ndipo amapukusa mitu yawo mondinyoza.+ Iwo amati:

  • Aheberi 11:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ena analandira mayesero awo mwa kutonzedwa ndi kukwapulidwa, komanso kuposa pamenepo, mwa maunyolo+ ndi ndende.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena