Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Mtengo wawo wa mpesa ndi wochokera ku mtengo wa mpesa wa ku Sodomu,

      Ndi kuminda ya m’mapiri a ku Gomora.+

      Zipatso zawo za mphesa ndi zakupha,

      Ndipo ndi zowawa.+

  • Rute 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma iye powayankha anali kunena kuti: “Musanditchulenso kuti Naomi,* muzinditchula kuti Mara,* chifukwa Wamphamvuyonse+ wachititsa moyo wanga kukhala wowawa kwambiri.+

  • Yobu 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mkwiyo wa Mulungu wandikhadzula. Iye ali nane chidani+

      Ndipo akundikukutira mano.+

      Mdani wanga akundiyang’ana ndi diso lozonda.+

  • Yobu 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mkwiyo wake nawonso wandiyakira,+

      Ndipo akungondiona ngati ndine mdani wake.

  • Yobu 33:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mulungu amapeza ponditsutsira,

      Amanditenga ngati mdani wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena