1 Samueli 4:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Mkaziyu atatsala pang’ono kumwalira, amayi amene anaima pambali pake anayamba kulankhula kuti: “Usachite mantha, pakuti wabereka mwana wamwamuna.”+ Koma iye sanayankhe kapena kuikirapo mtima. Salimo 39:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Zoonadi, munthu amayenda ngati chithunzithunzi.+Ndithudi, anthu amapokosera pachabe.+Munthu amaunjika zinthu ndipo sadziwa amene adzazitute.+ Mlaliki 9:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Komanso chikondi chawo, chidani chawo ndiponso nsanje yawo zatha kale,+ ndipo alibenso gawo mpaka kalekale pa chilichonse chimene chikuchitika padziko lapansi pano.+ Yesaya 63:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Inutu ndinu Atate wathu.+ Ngakhale kuti Abulahamu sanatidziwe ndipo Isiraeli sanatizindikire, inuyo Yehova ndinu Atate wathu. Dzina lanu ndinu Wotiwombola wakalekale.+
20 Mkaziyu atatsala pang’ono kumwalira, amayi amene anaima pambali pake anayamba kulankhula kuti: “Usachite mantha, pakuti wabereka mwana wamwamuna.”+ Koma iye sanayankhe kapena kuikirapo mtima.
6 Zoonadi, munthu amayenda ngati chithunzithunzi.+Ndithudi, anthu amapokosera pachabe.+Munthu amaunjika zinthu ndipo sadziwa amene adzazitute.+
6 Komanso chikondi chawo, chidani chawo ndiponso nsanje yawo zatha kale,+ ndipo alibenso gawo mpaka kalekale pa chilichonse chimene chikuchitika padziko lapansi pano.+
16 Inutu ndinu Atate wathu.+ Ngakhale kuti Abulahamu sanatidziwe ndipo Isiraeli sanatizindikire, inuyo Yehova ndinu Atate wathu. Dzina lanu ndinu Wotiwombola wakalekale.+