Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 31:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kodi amene anandipanga m’mimba si amene anapanganso iyeyo?+

      Kodi si mmodzi yemweyo amene anatipanga tonsefe m’mimba?

  • Salimo 127:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Taonani! Ana ndi cholowa chochokera kwa Yehova.+

      Chipatso cha mimba ndicho mphoto.+

  • Mlaliki 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Monga mmene munthu anabadwira kuchokera m’mimba mwa mayi ake, adzapitanso wamaliseche+ ngati mmene anabwerera, ndipo palibe chilichonse chimene adzatenge+ pa ntchito yake imene anaigwira mwakhama.

  • 1 Timoteyo 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pakuti sitinabwere ndi kanthu m’dziko, ndipo sitingatulukemo ndi kanthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena