Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 29:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Yehova ataona kuti Leya sanali kukondedwa kwenikweni, anam’patsa mphamvu zobereka,+ koma Rakele anali wosabereka.+

  • 1 Samueli 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 koma Hana anangom’patsa gawo limodzi. Komabe, iye anali kukonda kwambiri Hana+ ngakhale kuti Yehova anali atatseka mimba yake.+

  • Yobu 10:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kodi munanditulutsiranji m’mimba?+

      Zikanakhala bwino ndikanafa kuti diso ndi limodzi lomwe lisandione.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena