Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlaliki 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ine ndinafuna kumvetsetsa ndi kuganizira mozama zinthu zonsezi:+ Anthu olungama ndiponso anthu anzeru limodzi ndi ntchito zawo ali m’dzanja la Mulungu woona.+ Anthu sadziwa za chikondi kapena chidani chimene chinalipo iwo asanakhalepo.+

  • Maliro 3:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Tsopano ndani ananenapo kuti chinthu chichitike, chinthucho n’kuchitikadi Yehova asanalamule?+

  • Yakobo 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’malomwake, muyenera kunena kuti: “Yehova akalola,+ tikhala ndi moyo, ndi kuchita zakutizakuti.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena