Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndimakondwera ndi kuchita chifuniro chanu, inu Mulungu wanga,+

      Ndipo chilamulo chanu chili mumtima mwanga.+

  • Salimo 143:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndiphunzitseni kuchita chifuniro chanu,+

      Pakuti inu ndinu Mulungu wanga.+

      Mzimu wanu ndi wabwino.+

      Unditsogolere m’dziko la olungama.+

  • Yohane 4:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yesu anati: “Chakudya+ changa ndicho kuchita chifuniro+ cha amene anandituma ndi kutsiriza ntchito yake.+

  • Machitidwe 18:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 M’malomwake, anatsanzikana+ nawo ndi kuwauza kuti: “Yehova akalola ndidzabweranso kudzakuonani.”+ Choncho ananyamuka ku Efeso ulendo wa panyanja

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena