Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 112:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 112 Tamandani Ya, anthu inu!+

      א [ʼAʹleph]

      Wodala ndi munthu woopa Yehova,+

      ב [Behth]

      Munthu amene amasangalala kwambiri+ ndi malamulo ake.+

  • Yohane 4:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yesu anati: “Chakudya+ changa ndicho kuchita chifuniro+ cha amene anandituma ndi kutsiriza ntchito yake.+

  • Aroma 7:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mumtima mwanga+ ndimasangalala kwambiri+ ndi chilamulo cha Mulungu,

  • Aheberi 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 ananenanso kuti: “Taonani! Ine ndabwera kudzachita chifuniro chanu.”+ Akuchotsa dongosolo loyambalo kuti akhazikitse lachiwiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena